Salimo 25:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Moyo wake udzasangalala ndi ubwino wa Mulungu,+Mbadwa zake zidzatenga dziko lapansi kukhala lawo.+ Salimo 37:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Olungama adzalandira dziko lapansi,+Ndipo adzakhala mmenemo kwamuyaya.+ Yesaya 57:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ukamafuula popempha thandizo, zinthu zimene unasonkhanitsa sizidzakupulumutsa,+ koma mphepo idzaziulutsa zonsezo+ ndipo mpweya udzazitenga. Koma munthu wobisala mwa ine+ adzalandira dziko ndipo adzatenga phiri langa loyera.+ Yesaya 58:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 pamenepo mudzasangalala kwambiri mwa Yehova.+ Ine ndidzakuchititsani kuti mukwere m’malo okwezeka a dziko lapansi,+ ndipo ndidzakuchititsani kuti mudye zochokera m’cholowa cha Yakobo kholo lanu,+ pakuti pakamwa pa Yehova panena zimenezi.”+ Mateyu 5:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 “Odala ndi anthu amene ali ofatsa,+ chifukwa adzalandira dziko lapansi.+
13 Moyo wake udzasangalala ndi ubwino wa Mulungu,+Mbadwa zake zidzatenga dziko lapansi kukhala lawo.+
13 Ukamafuula popempha thandizo, zinthu zimene unasonkhanitsa sizidzakupulumutsa,+ koma mphepo idzaziulutsa zonsezo+ ndipo mpweya udzazitenga. Koma munthu wobisala mwa ine+ adzalandira dziko ndipo adzatenga phiri langa loyera.+
14 pamenepo mudzasangalala kwambiri mwa Yehova.+ Ine ndidzakuchititsani kuti mukwere m’malo okwezeka a dziko lapansi,+ ndipo ndidzakuchititsani kuti mudye zochokera m’cholowa cha Yakobo kholo lanu,+ pakuti pakamwa pa Yehova panena zimenezi.”+