Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndikomereni mtima, inu Yehova, chifukwa ndikulefuka.+

      Ndichiritseni,+ inu Yehova, chifukwa mafupa anga agwedezeka.

  • Salimo 31:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa cha chisoni, moyo wanga watha,+

      Ndipo chifukwa cha kuusa moyo kwanga, zaka zanga zafika kumapeto.+

      Chifukwa cha zolakwa zanga, mphamvu zanga zafooka,+

      Ndipo mafupa anga afooka.+

  • Salimo 41:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma ine ndinati: “Inu Yehova, ndikomereni mtima.+

      Ndichiritseni, pakuti ndakuchimwirani.”+

  • Salimo 51:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndichititseni kumva kufuula kokondwera ndi kosangalala,+

      Kuti munthu* amene mwamuthyola akondwere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena