Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Moyo wanga uli m’manja mwanu.+

      Ndilanditseni m’manja mwa adani anga ndi kwa anthu ondisakasaka.+

  • Yeremiya 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Inu Yehova mukudziwa bwino mavuto anga.+ Ndikumbukireni+ ndipo mutembenuke ndi kundiyang’ana kuti mubwezere anthu ondizunza.+ Musandichotsere moyo wanga chifukwa chakuti simupsa mtima mwamsanga.+ Onani chitonzo chimene chili pa ine chifukwa cha dzina lanu.+

  • Aroma 8:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Koma tikugonjetsa zinthu zonsezi+ kudzera mwa iye amene anatikonda.

  • 2 Akorinto 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Timazunzidwa, koma osati mochita kusowa kolowera.+ Timagwetsedwa pansi,+ koma sitiwonongedwa.+

  • 2 Petulo 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Chotero, zimenezi zikusonyeza kuti Yehova amadziwa kupulumutsa anthu odzipereka kwa iye akakhala pa mayesero.+ Koma anthu osalungama amawasungira tsiku loweruza kuti adzawawononge,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena