Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 37:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Wamphamvuyonse sitikumudziwa.+

      Iye ali ndi mphamvu zambiri,+

      Ndipo sadzanyoza+ chilungamo+ ndi kulungama kochuluka.+

  • Salimo 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu Yehova, mukhale wokwezeka mu mphamvu zanu.+

      Tidzaimba ndi kutamanda mphamvu zanu.+

  • Salimo 106:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Koma Mulungu anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake,+

      Kuti mphamvu zake zidziwike.+

  • Salimo 145:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo adzanena za ulemerero wa ufumu wanu.+

      Ndi kulankhula za mphamvu zanu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena