Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 145:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anthu adzanena za zochita zanu zamphamvu ndi zochititsa mantha.+

      Ndipo ine ndidzalengeza za ukulu wanu.+

  • Yeremiya 50:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 “Kukumveka phokoso la anthu amene akuthawa komanso amene apulumuka m’dziko la Babulo+ kuti akanene ku Ziyoni za chilango chimene Yehova Mulungu wathu akubwezera.+ Iye akubwezera kuwonongedwa kwa kachisi wake.+

  • Yeremiya 51:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova watichitira zinthu zachilungamo.+ Bwerani kuti tisimbe ntchito za Yehova Mulungu wathu mu Ziyoni.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena