Salimo 29:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 M’patseni Yehova, inu amphamvu,*M’patseni Yehova ulemerero ndipo vomerezani kuti iye ndi wamphamvu.+ Salimo 96:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Vomerezani Yehova, inu mabanja a mitundu ya anthu,+M’patseni Yehova ulemerero ndi kuvomereza kuti iye ndi wamphamvu.+
29 M’patseni Yehova, inu amphamvu,*M’patseni Yehova ulemerero ndipo vomerezani kuti iye ndi wamphamvu.+
7 Vomerezani Yehova, inu mabanja a mitundu ya anthu,+M’patseni Yehova ulemerero ndi kuvomereza kuti iye ndi wamphamvu.+