Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Vomerezani Yehova, inu mabanja a mitundu ya anthu,

      M’patseni Yehova ulemerero ndi kuvomereza kuti iye ndi wamphamvu.+

  • Salimo 96:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Vomerezani Yehova, inu mabanja a mitundu ya anthu,+

      M’patseni Yehova ulemerero ndi kuvomereza kuti iye ndi wamphamvu.+

  • Habakuku 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mulungu anabwera kuchokera ku Temani, Woyerayo anabwera kuchokera kuphiri la Parana.+ [Seʹlah.]+

      Ulemerero wake unaphimba kumwamba+ ndipo dziko lonse linamutamanda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena