Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 19:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iye waika abale anga enieni kutali ndi ine,+

      Ndipo ngakhale anthu ondidziwa andisiya.

  • Salimo 31:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndakhala chitonzo+ pamaso pa onse odana nane,+

      Ndipo kwa anthu oyandikana nawo ndakhala chitonzo chachikulu,+

      Kwa anthu ondidziwa ndakhala woopsa.+

      Akandiona ndili panja amandithawa.+

  • Mateyu 26:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Koma zonsezi zachitika kuti malemba a aneneri akwaniritsidwe.”+ Kenako ophunzira ake onse anamuthawa, n’kumusiya yekha.+

  • Yohane 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anabwera kudziko lakwawo, koma anthu akwawo enieniwo sanamulandire.+

  • Yohane 7:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Abale akewo+ sanali kumukhulupirira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena