Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Koma ine ndine nyongolotsi+ osati munthu.

      Anthu amanditonza ndipo ndine wonyozeka kwa anthu.+

  • Salimo 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Odana nane akunditonza kwambiri moti zikungokhala ngati mafupa anga aphwanyidwa,+

      Pakuti anthu akundifunsa tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Salimo 102:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Tsiku lonse adani anga amanditonza.+

      Anthu ondinyoza amagwiritsa ntchito dzina langa potemberera ena.+

  • Yesaya 53:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zoonadi, iye anatinyamulira matenda athu+ ndipo anatisenzera zowawa zathu.+ Koma ifeyo tinamuona ngati wosautsidwa,+ wokwapulidwa ndi Mulungu,+ ndiponso wozunzidwa.+

  • Aroma 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ngakhale Khristu sanadzikondweretse yekha,+ koma anachita mmene Malemba amanenera kuti: “Mnyozo wa anthu amene anali kukutonzani wagwa pa ine.”+

  • 1 Petulo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ngati anthu akukunyozani chifukwa cha dzina la Khristu,+ ndinu odala+ chifukwa zikusonyeza kuti mzimu waulemerero, umene ndi mzimu wa Mulungu, wakhazikika pa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena