Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndakhala chitonzo+ pamaso pa onse odana nane,+

      Ndipo kwa anthu oyandikana nawo ndakhala chitonzo chachikulu,+

      Kwa anthu ondidziwa ndakhala woopsa.+

      Akandiona ndili panja amandithawa.+

  • Salimo 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Odana nane akunditonza kwambiri moti zikungokhala ngati mafupa anga aphwanyidwa,+

      Pakuti anthu akundifunsa tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Salimo 74:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu Mulungu, kodi mdani adzakuchitirani mopanda ulemu kufikira liti?+

      Kodi mdani adzanyoza dzina lanu kwamuyaya?+

  • Salimo 79:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Anthu oyandikana nafe akutitonza,+

      Anthu otizungulira akutinyoza ndi kutiseka.+

  • Salimo 89:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Inu Yehova, kumbukirani mmene adani anu alankhulira motonza,+

      Mmene atonzera paliponse pamene mapazi a wodzozedwa wanu aponda.+

  • Aroma 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ngakhale Khristu sanadzikondweretse yekha,+ koma anachita mmene Malemba amanenera kuti: “Mnyozo wa anthu amene anali kukutonzani wagwa pa ine.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena