Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye adzauluka ngati loto, ndipo sadzam’peza.

      Adzathamangitsidwa ngati masomphenya a usiku.+

  • Salimo 90:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mwawawonongeratu,+ ndipo amangozimiririka ngati maloto.+

      M’mawa amakhala ngati msipu wobiriwira umene watsitsimuka.+

  • Yesaya 29:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Inde, zidzawachitikira ngati pamene munthu wanjala akulota kuti akudya, kenako n’kudzidzimuka n’kuona kuti m’mimba mwake mulibe kanthu,+ kapena ngati pamene munthu waludzu akulota kuti akumwa madzi, n’kudzidzimuka n’kuona kuti adakali wotopa ndipo kukhosi kwake n’kouma. Umu ndi mmene zidzachitikire ndi khamu lonse la mitundu imene ikuchita nkhondo ndi phiri la Ziyoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena