-
Yesaya 29:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Inde, zidzawachitikira ngati pamene munthu wanjala akulota kuti akudya, kenako n’kudzidzimuka n’kuona kuti m’mimba mwake mulibe kanthu,+ kapena ngati pamene munthu waludzu akulota kuti akumwa madzi, n’kudzidzimuka n’kuona kuti adakali wotopa ndipo kukhosi kwake n’kouma. Umu ndi mmene zidzachitikire ndi khamu lonse la mitundu imene ikuchita nkhondo ndi phiri la Ziyoni.+
-