Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kuti munthu wopanduka asalamulire,+

      Ndi kuti pasakhale misampha+ ya anthu.

  • Yobu 38:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuwala kwa oipa kumachotsedwa,+

      Ndipo dzanja lokwezedwa m’mwamba limathyoledwa.+

  • Salimo 37:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti manja a anthu oipa adzathyoledwa,+

      Koma Yehova adzathandiza anthu olungama.+

  • Ezekieli 30:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Iwe mwana wa munthu, ine ndidzathyola dzanja la Farao mfumu ya Iguputo.+ Dzanjalo silidzamangidwa ndi nsalu zomangira pachilonda+ kuti lichire n’kukhalanso lamphamvu kuti lizidzatha kugwira lupanga.”

  • Zekariya 11:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tsoka m’busa wanga wopanda pake+ amene akusiya nkhosa.+ Lupanga lidzamutema padzanja ndi kuboola diso lake la kudzanja lamanja. Dzanja lake lidzafota,+ ndipo diso lake la kudzanja lamanja lidzachita mdima.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena