Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Mafupa athu amwazika pakamwa pa Manda,

      Mofanana ndi zidutswa zimene zimamwazika pansi pamene munthu akuwaza ndi kung’amba mtengo.+

  • Yeremiya 14:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu amene akuwauza maulosi awowo, mitembo yawo idzatayidwa m’misewu ya Yerusalemu chifukwa cha njala ndi lupanga. Sipadzakhala wowaika m’manda, iwowo, akazi awo, ana awo aamuna ndi ana awo aakazi+ chifukwa ndidzawatsanulira tsoka pamutu pawo.’+

  • Yeremiya 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 ‘Iwo adzafa ndi matenda oopsa+ ndipo sadzawalira maliro+ kapena kuikidwa m’manda+ koma adzakhala ngati manyowa panthaka.+ Iwo adzafa ndi lupanga ndiponso njala yaikulu.+ Mitembo yawo idzakhala chakudya cha zolengedwa zouluka zam’mlengalenga ndi zilombo zakutchire.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena