Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 83:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo anawonongedwa ku Eni-dori.+

      Anasanduka manyowa a m’nthaka.+

  • Yesaya 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 N’chifukwa chake mkwiyo wa Yehova wayakira anthu ake ndipo adzatambasula dzanja lake n’kuwapha.+ Mapiri adzanjenjemera+ ndipo mitembo yawo idzakhala ngati zinyalala m’misewu.+

      Chifukwa cha zonsezi, mkwiyo wake sunabwerere, ndipo dzanja lake lidakali lotambasula.

  • Yeremiya 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mafupawo adzawamwaza poyera ndipo dzuwa, mwezi, ndi makamu onse akumwamba zidzawala pa iwo. Zinthu zimenezi ndi zimene iwo anali kuzikonda, kuzitumikira, kuzitsatira,+ kuzipembedza, ndi kuziweramira.+ Mafupawo sadzasonkhanitsidwa pamodzi kapena kuikidwa m’manda. Iwo adzakhala ngati manyowa panthaka.”+

  • Yeremiya 9:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Unene kuti, ‘Yehova wanena kuti: “Mitembo ya anthu idzangoti mbwee panthaka ngati manyowa. Idzakhala ngati tirigu amene angomumweta kumene koma palibe munthu womusonkhanitsa pamodzi.”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena