Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndani anatseka nyanja ndi zitseko,+

      Imene inayamba kuyenda ngati kuti ikutumphuka m’mimba?

  • Salimo 107:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iye amachititsa mphepo yamkuntho kukhala bata,+

      Moti mafunde a panyanja amadekha.+

  • Yeremiya 31:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yehova ndiye Wopereka dzuwa kuti liziwala masana,+ woikira mwezi malamulo,+ wopereka nyenyezi+ kuti ziziwala usiku,+ amene amavundula nyanja kuti mafunde ake achite phokoso.+ Wochita zimenezi dzina lake ndi Yehova wa makamu.+ Iye wanena kuti:

  • Nahumu 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Amadzudzula nyanja+ ndi kuiphwetsa ndipo amaumitsa mitsinje yonse.+

      Basana ndi Karimeli afota+ ndipo maluwa a mitengo ya ku Lebanoni nawonso afota.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena