Yobu 30:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Pakuti ndikudziwa bwino kuti mudzandibwezera ku imfa,+Kunyumba yosonkhanako aliyense wamoyo. Salimo 49:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kuti akhale ndi moyo mpaka muyaya osaona dzenje la manda.+ Mlaliki 3:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Pakuti ana a anthu ali ndi mapeto, ndipo zinyamanso zili ndi mapeto. Mapeto a zonsezi ndi ofanana.+ Nyama imafa ndipo munthunso amafa.+ Mzimu wa zonsezi ndi umodzi,+ moti munthu saposa nyama, pakuti zonse n’zachabechabe. Mlaliki 9:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+ Aheberi 11:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Mwa chikhulupiriro, Inoki+ anasamutsidwa kuti asafe mozunzika, moti sanapezeke kwina kulikonse chifukwa Mulungu anamusamutsa.+ Pakuti asanasamutsidwe, Mulungu anamuchitira umboni kuti akukondwera naye.+
19 Pakuti ana a anthu ali ndi mapeto, ndipo zinyamanso zili ndi mapeto. Mapeto a zonsezi ndi ofanana.+ Nyama imafa ndipo munthunso amafa.+ Mzimu wa zonsezi ndi umodzi,+ moti munthu saposa nyama, pakuti zonse n’zachabechabe.
5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+
5 Mwa chikhulupiriro, Inoki+ anasamutsidwa kuti asafe mozunzika, moti sanapezeke kwina kulikonse chifukwa Mulungu anamusamutsa.+ Pakuti asanasamutsidwe, Mulungu anamuchitira umboni kuti akukondwera naye.+