Salimo 40:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chilungamo chanu sindinachibise mumtima mwanga.+Ndinalengeza za kukhulupirika kwanu ndi chipulumutso chanu.+Sindinabise kukoma mtima kwanu kosatha ndi choonadi chanu mumpingo waukulu.”+ Salimo 71:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Pakamwa panga padzanena za chilungamo chanu,+Padzanena za chipulumutso chanu tsiku lonse,+Pakuti ntchito za chilungamo ndi chipulumutso chanu ndi zochuluka ndipo sindinathe kuziwerenga.+ Yesaya 52:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mapazi+ a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino, ndi okongola kwabasi!+ Munthu yemwe akulengeza za mtendere,+ yemwe akubweretsa uthenga wabwino wa zinthu zabwino kuposa kale,+ yemwe akulengeza za chipulumutso,+ yemwe akuuza Ziyoni kuti: “Mulungu wako wakhala mfumu.”+ Machitidwe 13:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 “Amuna inu, abale anga, inu ana a mbadwa za Abulahamu, ndi ena onse oopa Mulungu amene ali pakati panu, mawu a chipulumutso chimenechi atumizidwa kwa ife.+
10 Chilungamo chanu sindinachibise mumtima mwanga.+Ndinalengeza za kukhulupirika kwanu ndi chipulumutso chanu.+Sindinabise kukoma mtima kwanu kosatha ndi choonadi chanu mumpingo waukulu.”+
15 Pakamwa panga padzanena za chilungamo chanu,+Padzanena za chipulumutso chanu tsiku lonse,+Pakuti ntchito za chilungamo ndi chipulumutso chanu ndi zochuluka ndipo sindinathe kuziwerenga.+
7 Mapazi+ a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino, ndi okongola kwabasi!+ Munthu yemwe akulengeza za mtendere,+ yemwe akubweretsa uthenga wabwino wa zinthu zabwino kuposa kale,+ yemwe akulengeza za chipulumutso,+ yemwe akuuza Ziyoni kuti: “Mulungu wako wakhala mfumu.”+
26 “Amuna inu, abale anga, inu ana a mbadwa za Abulahamu, ndi ena onse oopa Mulungu amene ali pakati panu, mawu a chipulumutso chimenechi atumizidwa kwa ife.+