1 Samueli 14:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Kenako anthu amene anali kutchire mumsasa ndi anthu onse kumudzi wa asilikaliwo anayamba kunjenjemera.+ Anthu olanda katundu+ nawonso anali kunjenjemera, ndipo nthaka inayamba kugwedezeka.+ Zimenezi zinali zochokera kwa Mulungu.+ Yobu 9:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Amachititsa dziko lapansi kunjenjemera pamalo ake,Mwakuti zipilala+ zake zimagwedezeka. Salimo 82:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Milunguyo siikudziwa kanthu ndipo siikuzindikira.+Ikuyendayenda mu mdima,+Ndipo maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.+ Ezekieli 38:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 ‘Ine ndidzalankhula mwaukali wanga+ woyaka moto komanso nditakwiya kwambiri.+ Ndithudi, pa tsikulo m’dziko la Isiraeli mudzachitika chivomezi chachikulu.+
15 Kenako anthu amene anali kutchire mumsasa ndi anthu onse kumudzi wa asilikaliwo anayamba kunjenjemera.+ Anthu olanda katundu+ nawonso anali kunjenjemera, ndipo nthaka inayamba kugwedezeka.+ Zimenezi zinali zochokera kwa Mulungu.+
5 Milunguyo siikudziwa kanthu ndipo siikuzindikira.+Ikuyendayenda mu mdima,+Ndipo maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.+
19 ‘Ine ndidzalankhula mwaukali wanga+ woyaka moto komanso nditakwiya kwambiri.+ Ndithudi, pa tsikulo m’dziko la Isiraeli mudzachitika chivomezi chachikulu.+