Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kwa nyama iliyonse yam’tchire ya padziko lapansi, ndi kwa cholengedwa chilichonse chouluka m’mlengalenga, komanso kwa chokwawa chilichonse cha padziko lapansi chimene chili ndi moyo, ndapereka zomera zonse kuti zikhale chakudya chawo.”+ Ndipo zinaterodi.

  • 1 Mafumu 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno Ahabu anauza Obadiya kuti: “Pita m’dzikoli, ukayendere akasupe onse a madzi ndi zigwa* zonse. Mwina tikhoza kupeza udzu wobiriwira+ woti tidyetse mahatchi ndi nyulu, kuti nyamazi zisapitirize kufa.”+

  • Yeremiya 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mbidzi+ zangoima chilili m’mapiri opanda kanthu. Zikupuma mwawefuwefu ngati mimbulu. Maso awo achita mdima chifukwa kulibe msipu.+

  • Yoweli 2:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Inu zilombo zakutchire musachite mantha,+ pakuti malo odyetserako ziweto a m’chipululu adzamera msipu wobiriwira.+ Mitengo nayonso idzabereka zipatso.+ Mtengo wa mkuyu ndi mtengo wa mpesa udzatulutsa zipatso zake zonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena