Genesis 1:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Tsopano Mulungu anati: “Taonani, ndakupatsani zomera zonse zobala mbewu zapadziko lonse lapansi, ndi mitengo yonse yobala zipatso za mbewu+ kuti zikhale chakudya chanu.+ Genesis 3:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Minga ndi zitsamba zobaya* zidzamera panthaka,+ ndipo udzadya zomera za m’nthaka. Genesis 9:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Nyama yamoyo iliyonse ikhale chakudya chanu.+ Komanso ndikukupatsani zamasamba zonse kuti zikhale chakudya chanu.+ Yobu 38:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Kuti inyowetse malo owonongeka ndi mvula yamkuntho ndiponso ouma,Komanso kuti imeretse udzu?+ Aheberi 6:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mwachitsanzo, nthaka imamwa madzi a mvula imene imagwera panthakapo kawirikawiri. Kenako imatulutsa zomera zimene zimapindulitsa amene ailima.+ Nthaka imeneyi imalandiranso dalitso kuchokera kwa Mulungu.
29 Tsopano Mulungu anati: “Taonani, ndakupatsani zomera zonse zobala mbewu zapadziko lonse lapansi, ndi mitengo yonse yobala zipatso za mbewu+ kuti zikhale chakudya chanu.+
3 Nyama yamoyo iliyonse ikhale chakudya chanu.+ Komanso ndikukupatsani zamasamba zonse kuti zikhale chakudya chanu.+
7 Mwachitsanzo, nthaka imamwa madzi a mvula imene imagwera panthakapo kawirikawiri. Kenako imatulutsa zomera zimene zimapindulitsa amene ailima.+ Nthaka imeneyi imalandiranso dalitso kuchokera kwa Mulungu.