Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ulamuliro wake umakhala ngati kuwala kwa m’mawa pamene dzuwa lawala,+

      M’mawa wopanda mitambo.

      Umakhala ngati msipu womera padziko mvula ikakata, dzuwa n’kuwala.’+

  • Nahumu 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Alonda ako ali ngati dzombe ndipo akapitawo ako olemba anthu usilikali ali ngati gulu la dzombe. Pa tsiku lozizira limabisala m’makoma. Dzuwa likawala, dzombelo limauluka ndi kuthawira kutali ndipo silidziwika kuti lili kuti.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena