Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Malangizo anga adzagwa ngati mvula,+

      Mawu anga adzatsika ngati mame,+

      Ngati mvula yowaza pa udzu,+

      Ngatinso mvula yamphamvu pazomera.+

  • Deuteronomo 33:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Lidalitsidwenso ndi zinthu zabwino kwambiri, zochokera ku dzuwa,+

      Ndi zinthu zabwino kwambiri, zokolola za miyezi yosiyanasiyana,+

  • Salimo 72:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Adzatsika ngati mvula pa udzu umene wadulidwa,+

      Ngati mvula yambiri yamvumbi imene imanyowetsa kwambiri nthaka.+

  • Yesaya 55:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti monga momwe mvula ndi chipale chofewa zimagwera kuchokera kumwamba, osabwereranso kumeneko mpaka zitanyowetsa kwambiri nthaka n’kumeretsa zomera ndi kuzibereketsa,+ wobzala mbewu n’kupatsidwa zokolola komanso wakudya n’kupatsidwa chakudya,+

  • Mika 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Otsala a Yakobo,+ pakati pa mitundu yambiri ya anthu, adzakhala ngati mame ochokera kwa Yehova.+ Iwo adzakhala ngati mvula yamvumbi imene ikuwaza pazomera,+ yomwe sidalira munthu kapena kuyembekezera ana a anthu ochokera kufumbi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena