Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova amasanthula anthu olungama ndi oipa omwe,+

      Ndipo Mulungu amadana kwambiri ndi aliyense wokonda chiwawa.+

  • Salimo 16:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndidzatamanda Yehova amene wandipatsa malangizo.+

      Ndithudi, usiku impso zanga zandiwongolera.+

  • 1 Akorinto 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pakuti sindikudziwa+ kanthu kalikonse konditsutsa mumtima mwanga. Koma zimenezi sizikutanthauza kuti basi ndine wolungama, koma Yehova ndiye amandifufuza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena