Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma ine ndasautsika ndipo ndasauka.+

      Yehova amandiwerengera.+

      Inu ndinu thandizo langa ndi Wopereka chipulumutso kwa ine.+

      Inu Mulungu wanga musachedwe.+

  • Salimo 86:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 86 Tcherani khutu inu Yehova. Ndiyankheni,+

      Pakuti ndasautsika ndipo ndasauka.+

  • 2 Akorinto 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pakuti mukudziwa kukoma mtima kwakukulu kwa Ambuye wathu Yesu Khristu, kuti ngakhale kuti iye anali wolemera, anakhala wosauka chifukwa cha inu,+ kuti inuyo mulemere+ kudzera m’kusauka kwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena