Salimo 119:125 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 125 Ine ndine mtumiki wanu.+ Ndithandizeni kukhala wozindikira,+Kuti ndidziwe zikumbutso zanu.+ Salimo 143:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Adani anga muwakhalitse chete monga mwa kukoma mtima kwanu kosatha.+Ndipo muwononge onse ondichitira zoipa,+Pakuti ine ndine mtumiki wanu.+
12 Adani anga muwakhalitse chete monga mwa kukoma mtima kwanu kosatha.+Ndipo muwononge onse ondichitira zoipa,+Pakuti ine ndine mtumiki wanu.+