Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Akakhala pampando wachifumu, ayenera kukopera buku lakelake la chilamulo ichi, kuchokera m’buku limene ansembe achilevi amasunga.+

  • Salimo 119:105
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 105 Mawu anu ndi nyale younikira kumapazi anga,+

      Ndi kuwala kounikira njira yanga.+

  • Miyambo 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 mukungonyalanyaza malangizo anga onse,+ ndipo simunamvere kudzudzula kwanga,+

  • 2 Timoteyo 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Malemba onse anauziridwa ndi Mulungu,+ ndipo ndi opindulitsa pa kuphunzitsa,+ kudzudzula,+ kuwongola zinthu+ ndi kulangiza m’chilungamo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena