Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 17
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 17:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 22:20; De 15:21; Mki 1:8

Deuteronomo 17:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:23; 13:6; Owe 2:20

Deuteronomo 17:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:19; Yer 8:2; Eze 8:16
  • +Yer 7:18; 19:5

Deuteronomo 17:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:14; Yoh 7:51

Deuteronomo 17:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:10

Deuteronomo 17:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:30; Mt 18:16; Yoh 8:17; 2Ak 13:1; 1Ti 5:19; Ahe 10:28
  • +De 19:15

Deuteronomo 17:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:9
  • +De 13:5; 1Ak 5:13

Deuteronomo 17:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:17
  • +Nu 35:11
  • +1Mf 3:28; Yes 1:17; Yer 5:28
  • +1Mf 3:16
  • +De 12:5; Sl 122:2, 5

Deuteronomo 17:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:17; 21:5; Hag 2:11; Mki 2:7
  • +1Sa 7:16
  • +De 19:17; 21:5

Deuteronomo 17:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mki 2:7
  • +De 5:32; 12:32; Yos 1:7; Miy 4:27

Deuteronomo 17:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 19:13; Miy 11:2; Ho 4:4
  • +Ahe 10:28
  • +De 13:5; 1Ak 5:13

Deuteronomo 17:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 15:31; De 13:11; 19:20

Deuteronomo 17:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:1; Yos 1:3; Sl 44:2
  • +1Sa 8:5, 20; 10:19

Deuteronomo 17:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 9:17; 10:24; 16:12

Deuteronomo 17:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 20:1; 2Sa 8:4; Sl 20:7; Miy 21:31
  • +Yes 31:1; 36:9; Eze 17:15

Deuteronomo 17:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 11:3; Ne 13:26
  • +Yob 31:24; Sl 62:10; 1Ti 6:9

Deuteronomo 17:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 31:9, 26; 2Mf 22:8

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    3/15/2007, tsa. 20

    5/1/1995, ptsa. 12-13

Deuteronomo 17:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 34:18
  • +De 11:18; Sl 1:2; 119:97

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/2002, ptsa. 12-17

    10/1/2000, tsa. 8

    5/1/1995, ptsa. 12-13

Deuteronomo 17:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 15:17; 2Mb 32:25; Sl 131:1; Mko 10:42; 1Pe 5:5
  • +De 5:32; 1Sa 13:13; 1Mf 15:5
  • +Miy 10:27

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/1995, ptsa. 12-13

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 17:1Le 22:20; De 15:21; Mki 1:8
Deut. 17:2De 4:23; 13:6; Owe 2:20
Deut. 17:3De 4:19; Yer 8:2; Eze 8:16
Deut. 17:3Yer 7:18; 19:5
Deut. 17:4De 13:14; Yoh 7:51
Deut. 17:5De 13:10
Deut. 17:6Nu 35:30; Mt 18:16; Yoh 8:17; 2Ak 13:1; 1Ti 5:19; Ahe 10:28
Deut. 17:6De 19:15
Deut. 17:7De 13:9
Deut. 17:7De 13:5; 1Ak 5:13
Deut. 17:8De 1:17
Deut. 17:8Nu 35:11
Deut. 17:81Mf 3:28; Yes 1:17; Yer 5:28
Deut. 17:81Mf 3:16
Deut. 17:8De 12:5; Sl 122:2, 5
Deut. 17:9De 19:17; 21:5; Hag 2:11; Mki 2:7
Deut. 17:91Sa 7:16
Deut. 17:9De 19:17; 21:5
Deut. 17:11Mki 2:7
Deut. 17:11De 5:32; 12:32; Yos 1:7; Miy 4:27
Deut. 17:12Sl 19:13; Miy 11:2; Ho 4:4
Deut. 17:12Ahe 10:28
Deut. 17:12De 13:5; 1Ak 5:13
Deut. 17:13Nu 15:31; De 13:11; 19:20
Deut. 17:14De 7:1; Yos 1:3; Sl 44:2
Deut. 17:141Sa 8:5, 20; 10:19
Deut. 17:151Sa 9:17; 10:24; 16:12
Deut. 17:16De 20:1; 2Sa 8:4; Sl 20:7; Miy 21:31
Deut. 17:16Yes 31:1; 36:9; Eze 17:15
Deut. 17:171Mf 11:3; Ne 13:26
Deut. 17:17Yob 31:24; Sl 62:10; 1Ti 6:9
Deut. 17:18De 31:9, 26; 2Mf 22:8
Deut. 17:192Mb 34:18
Deut. 17:19De 11:18; Sl 1:2; 119:97
Deut. 17:201Sa 15:17; 2Mb 32:25; Sl 131:1; Mko 10:42; 1Pe 5:5
Deut. 17:20De 5:32; 1Sa 13:13; 1Mf 15:5
Deut. 17:20Miy 10:27
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 17:1-20

Deuteronomo

17 “Usapereke kwa Yehova Mulungu wako nsembe ya ng’ombe kapena nkhosa yokhala ndi chilema kapena vuto lililonse, chifukwa zimenezi ndi zonyansa kwa Yehova Mulungu wako.+

2 “Pakati panu pakapezeka mwamuna kapena mkazi wochita zinthu zoipa pamaso pa Yehova Mulungu wanu, mu umodzi mwa mizinda yanu imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, ndipo akuphwanya pangano la Mulungu,+ 3 moti akupita kukalambira milungu ina ndi kuigwadira, kapena kugwadira dzuwa, mwezi kapena khamu lonse la zinthu zakuthambo,+ chinthu chimene ine sindinakulamuleni,+ 4 ndipo inu mwamva mutauzidwa, ndiponso mutafufuza mwatsimikizira kuti ndi zoona,+ chinthu choipachi chachitikadi mu Isiraeli, 5 muzitulutsira mwamuna kapena mkazi wochita chinthu choipayo kunja kwa mzinda, ndipo muzim’ponya miyala kuti afe.+ 6 Munthuyo aziphedwa mutamva umboni wa pakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu.+ Asaphedwe chifukwa cha umboni wa munthu mmodzi.+ 7 Dzanja la mbonizo lizikhala loyamba kum’ponya miyala kuti afe, ndipo anthu ena onse azibwera pambuyo.+ Choncho muzichotsa woipayo pakati panu.+

8 “Mlandu wofuna chigamulo ukakukulira kwambiri,+ monga mlandu wokhudza kukhetsa magazi,+ mlandu umene munthu wakasuma,+ mlandu wokhudza zachiwawa kapena mkangano+ umene wachitika mumzinda wanu, pamenepo uzinyamuka ndi kupita kumalo amene Yehova Mulungu wako adzasankhe.+ 9 Uzipita kwa ansembe+ achilevi ndi kwa woweruza+ amene aziweruza m’masiku amenewo. Uziwafotokozera nkhaniyo ndipo iwo azikuuza chigamulo.+ 10 Zimene akuuza kumalo amene Yehova adzasankhe uzichita zomwezo. Uzionetsetsa kuti ukuchita zonse zimene akulangiza. 11 Uzichita mogwirizana ndi chilamulo chimene akupatsa ndi chigamulo chimene akuuza.+ Usapatukire kudzanja lamanja kapena lamanzere pa mawu amene akupatsa.+ 12 Munthu amene adzadzikuza mwa kusamvera wansembe amene akutumikira Yehova Mulungu wako kapena mwa kusamvera woweruza,+ munthu ameneyo afe ndithu.+ Muzichotsa woipayo mu Isiraeli.+ 13 Anthu onse adzamva zimenezo ndi kuchita mantha+ ndipo sadzadzikuzanso.

14 “Ukakafika m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, n’kulitengadi kukhala lako ndi kukhalamo,+ pamenepo iwe n’kunena kuti, ‘Ndidziikire mfumu ngati mitundu ina yonse yondizungulira,’+ 15 uzidziikira mfumu imene Yehova Mulungu wako adzasankhe.+ Mfumu imene udzadziikire idzachokere pakati pa abale ako. Sudzaloledwa kudziikira mlendo amene si m’bale wako kukhala mfumu. 16 Koma asadzichulukitsire mahatchi+ kapena kuchititsa anthu kubwerera ku Iguputo kuti akakhale ndi mahatchi ochuluka+ pakuti Yehova wakuuzani kuti, ‘Musabwererenso kudzera njira iyi.’ 17 Asachulukitsenso akazi kuti mtima wake ungapatuke,+ ndipo asachulukitsenso kwambiri siliva ndi golide wake.+ 18 Akakhala pampando wachifumu, ayenera kukopera buku lakelake la chilamulo ichi, kuchokera m’buku limene ansembe achilevi amasunga.+

19 “Buku limeneli azikhala nalo nthawi zonse ndipo aziliwerenga masiku onse a moyo wake,+ kuti aphunzire kuopa Yehova Mulungu wake ndi kusunga mawu onse a chilamulo ichi, kutinso azitsatira malangizo ake.+ 20 Azichita zimenezi kuti mtima wake usadzikweze pamaso pa abale ake,+ komanso kuti asachoke pachilamulo mwa kupatukira kudzanja lamanja kapena lamanzere.+ Azichita zimenezi kuti iyeyo ndi ana ake atalikitse masiku a ufumu wawo+ mu Isiraeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena