Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mphepo,+

      Ndiponso kuti diso langa silidzaonanso zabwino.

  • Salimo 39:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 “Inu Yehova, ndidziwitseni za kufulumira kwa chimaliziro changa,+

      Ndiponso kuti masiku anga ndi ochepa motani,+

      Kuti ndidziwe kufupika kwa moyo wanga.+

  • Salimo 89:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Kumbukirani utali wa moyo wanga.+

      Kodi ana onse a anthu munawalenga pachabe?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena