Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Munthu wobadwa kwa mkazi,+

      Amakhala ndi moyo waufupi,+ wodzaza ndi masautso.+

  • Salimo 144:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Munthu amafanana ndi mpweya wotuluka m’mphuno.+

      Masiku ake ali ngati mthunzi wongodutsa.+

  • Mlaliki 11:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ngakhale munthu atakhala ndi moyo zaka zambiri, m’zaka zonsezo azisangalala.+ Iye akumbukire masiku a mdima,+ ngakhale atakhala ambiri. Tsiku lililonse limene likubwera n’lachabechabe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena