Salimo 39:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Taonani! Mwachepetsa masiku anga.+Ndipo nthawi ya moyo wanga si kanthu pamaso panu.+Ndithudi, munthu aliyense ngakhale atakhala wamphamvu bwanji, sali kanthu koma ali ngati mpweya wotuluka m’mphuno.+ [Seʹlah.] Salimo 62:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndithudi, ana a anthu ochokera kufumbi ali ngati mpweya,+Ana a anthu ndi malo othawirako achinyengo.+Onse pamodzi akaikidwa pasikelo ndi opepuka kuposa mpweya.+
5 Taonani! Mwachepetsa masiku anga.+Ndipo nthawi ya moyo wanga si kanthu pamaso panu.+Ndithudi, munthu aliyense ngakhale atakhala wamphamvu bwanji, sali kanthu koma ali ngati mpweya wotuluka m’mphuno.+ [Seʹlah.]
9 Ndithudi, ana a anthu ochokera kufumbi ali ngati mpweya,+Ana a anthu ndi malo othawirako achinyengo.+Onse pamodzi akaikidwa pasikelo ndi opepuka kuposa mpweya.+