Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Zonsezi zimayembekezera inu+

      Kuti muzipatse chakudya pa nyengo yake.+

  • Salimo 145:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zolengedwa zonse zimayang’ana kwa inu mwachiyembekezo,+

      Ndipo mumazipatsa chakudya pa nyengo yake.+

  • Salimo 147:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iye amapatsa zilombo chakudya chawo,+

      Amapatsanso ana a makwangwala chakudya chimene amalirira.+

  • Mateyu 5:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba.+ Chifukwa iye amawalitsira dzuwa lake pa anthu oipa ndi abwino, ndi kuvumbitsira mvula anthu olungama ndi osalungama omwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena