Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Popeza kuti ndine wogwirizana ndi Mulungu,+ ndidzatamanda mawu ake.

      Popeza kuti ndine wogwirizana ndi Yehova, ndidzatamanda mawu ake.+

  • Yesaya 42:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa cha chilungamo chake,+ Yehova walemekeza ndi kukweza malamulo ake mokondwera.+

  • Aheberi 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mofanana ndi zimenezi, Mulungu pofuna kuwatsimikizira kwambiri anthu olandira lonjezolo monga cholowa chawo,+ kuti chifuniro chake n’chosasinthika,+ anachita kulumbira pa zimene analonjezazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena