Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Wodala ndi mtundu umene Mulungu wawo ndi Yehova,+

      Anthu amene iye wawasankha kukhala cholowa chake.+

  • Salimo 46:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova wa makamu ali ndi ife.+

      Mulungu wa Yakobo ndiye malo athu okwezeka ndiponso achitetezo.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 144:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Odala ndi anthu amene zimenezi zikuwachitikira.”

      Ayi, koma odala ndi anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova.+

  • Yeremiya 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Wodala ndi munthu aliyense amene amakhulupirira Yehova, amene amadalira Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena