Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 16:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mudzandidziwitsa njira ya moyo.+

      Chifukwa cha nkhope yanu, munthu adzakondwera mokwanira.+

      Kudzanja lanu lamanja kuli chimwemwe mpaka muyaya.+

  • Salimo 45:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Umakonda chilungamo+ ndipo umadana ndi zoipa.+

      N’chifukwa chake Mulungu, Mulungu wako,+ wakudzoza+ ndi mafuta achikondwerero chachikulu+ kuposa cha mafumu ena.+

  • Machitidwe 2:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mwandidziwitsa njira za moyo, ndipo chifukwa cha nkhope yanu ndidzakhala ndi chimwemwe chosefukira.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena