Salimo 25:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Inu Mulungu wanga, chikhulupiriro changa chili mwa inu.+Musalole kuti ndichite manyazi.Adani anga asakondwere chifukwa cha masautso anga.+ Salimo 69:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Onse amene akuyembekezera inu asachite manyazi chifukwa cha ine,+Inu Ambuye Wamkulu Koposa, Yehova wa makamu.+Onse amene akufunafuna inu, asanyazitsidwe chifukwa cha ine,+Inu Mulungu wa Isiraeli.+ Yesaya 50:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzandithandiza.+ N’chifukwa chake sindidzamva kuti ndanyozeka. Pa chifukwa chimenechi ndalimbitsa nkhope yanga ngati mwala wa nsangalabwi, ndipo ndikudziwa kuti sindidzachita manyazi.+ Mateyu 27:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Cha m’ma 3 kolokomo Yesu anafuula mwamphamvu kuti: “Eʹli, Eʹli, laʹma sa·bach·thaʹni?” kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine?”+
2 Inu Mulungu wanga, chikhulupiriro changa chili mwa inu.+Musalole kuti ndichite manyazi.Adani anga asakondwere chifukwa cha masautso anga.+
6 Onse amene akuyembekezera inu asachite manyazi chifukwa cha ine,+Inu Ambuye Wamkulu Koposa, Yehova wa makamu.+Onse amene akufunafuna inu, asanyazitsidwe chifukwa cha ine,+Inu Mulungu wa Isiraeli.+
7 Koma Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzandithandiza.+ N’chifukwa chake sindidzamva kuti ndanyozeka. Pa chifukwa chimenechi ndalimbitsa nkhope yanga ngati mwala wa nsangalabwi, ndipo ndikudziwa kuti sindidzachita manyazi.+
46 Cha m’ma 3 kolokomo Yesu anafuula mwamphamvu kuti: “Eʹli, Eʹli, laʹma sa·bach·thaʹni?” kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine?”+