Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 32:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Atumiki a Senakeribuwo analankhula zinthu zinanso zonyoza Yehova Mulungu woona+ ndi Hezekiya mtumiki wake.

  • Mateyu 10:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Wophunzira amangofanana ndi mphunzitsi wake, ndipo kapolo amangofanana ndi mbuye wake.+ Ngati anthu atchula mwininyumba kuti Belezebule,*+ kuli bwanji ena a m’banja lakelo, kodi sadzawanena zoposa pamenepa?

  • Machitidwe 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Paulo atafika, Ayuda amene anabwera kuchokera ku Yerusalemu, anaima momuzungulira n’kumamuneneza milandu yoopsa yambiri,+ imene sanathe kupereka umboni wake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena