Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pakuti pa tsiku la tsoka, iye adzandibisa m’malo ake otetezeka.+

      Adzandibisa m’malo obisika m’hema wake.+

      Adzandiika pamwamba, pathanthwe.+

  • Salimo 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndinu malo anga obisalamo, mudzanditeteza ku masautso.+

      Mudzachititsa kuti chisangalalo chindizungulire pamene mukundipulumutsa.+ [Seʹlah.]

  • Machitidwe 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Chotero lapani+ ndi kutembenuka+ kuti machimo anu afafanizidwe,+ ndiponso kuti nyengo zotsitsimutsa+ zibwere kuchokera kwa Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena