Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pakuti anthu oipa adzatheratu onse,+

      Ndipo adani a Yehova adzafanana ndi busa la msipu wobiriwira mochititsa kaso.

      Iwo adzatha.+ Adzazimiririka ndi kusanduka utsi.+

  • Salimo 104:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ochimwa adzafafanizidwa padziko lapansi.+

      Ndipo anthu oipa sadzakhalaponso.+

      Tamanda Yehova, iwe moyo wanga. Tamandani Ya, anthu inu!*+

  • Miyambo 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Anthu akamakumbukira zabwino zimene munthu wolungama anali kuchita, amam’dalitsa,+ koma dzina la anthu oipa lidzawola.+

  • Mateyu 25:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Ndipo iwowa adzachoka kupita ku chiwonongeko chotheratu,+ koma olungama ku moyo wosatha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena