Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mwadzikweza pamaso pa Ambuye wakumwamba+ ndipo anthu akubweretserani ziwiya za m’nyumba yake.+ Inuyo, nduna zanu, adzakazi anu ndi akazi anu ena apambali mwamwera vinyo m’ziwiya zimenezi. Mwatamanda milungu wamba yasiliva, yagolide, yamkuwa, yachitsulo, yamitengo ndi yamiyala+ imene siona, kumva kapena kudziwa kalikonse.+ Koma Mulungu amene amasunga mpweya wanu+ ndi njira zanu zonse m’dzanja lake,+ simunamulemekeze.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena