2 Koma Yehova anakhalabe ndi Yosefe, ndipo iye anakhala wopambana m’zochita zake zonse.+ Anakhalanso munthu waudindo m’nyumba ya mbuye wake, Mwiguputoyo.
2 Wantchito wochita zinthu mozindikira, adzalamulira mwana wa mbuye wake amene amachita zinthu zochititsa manyazi,+ ndipo adzalandira nawo cholowa pamodzi ndi ana a mbuye wake.+