Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti amadzinyenga yekha,+

      Ndipo sazindikira cholakwa chake ndi kudana nacho.+

  • Yesaya 65:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iwo amanena kuti, ‘Khala pawekha. Usandiyandikire, kuti ndingakupatsire chiyero changa.’+ Iwo ali ngati utsi m’mphuno mwanga,+ ngati moto woyaka tsiku lonse.+

  • Luka 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo iye anawauza kuti: “Inu mumadzitcha olungama pamaso pa anthu,+ koma Mulungu akudziwa mitima yanu.+ Chifukwa chimene chili chapamwamba kwa anthu n’chonyansa m’maso mwa Mulungu.+

  • 2 Timoteyo 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 achiwembu,+ osamva za ena, odzitukumula ndiponso onyada,+ okonda zosangalatsa, m’malo mokonda Mulungu,+

  • 1 Yohane 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tikanena kuti: “Tilibe uchimo,”+ ndiye kuti tikudzinamiza+ ndipo mwa ife mulibe choonadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena