Genesis 24:60 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 60 Ndiyeno iwo anayamba kudalitsa Rabeka kuti: “Iwe mlongo wathu, ukakhale mayi wa anthu masauzande kuchulukitsa ndi masauzande 10, ndipo mbewu yako ikalande mizinda ya adani awo.”+ Oweruza 5:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Anthu okhala m’midzi anachoka m’midzi yawo, anachoka m’midzi ya Isiraeli,+Kufikira pamene ine Debora+ ndinauka,Kufikira pamene ine ndinauka monga mayi mu Isiraeli.+ Aroma 2:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Koma Myuda ndi amene ali wotero mkati,+ ndipo mdulidwe wake ndi wa mumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo satamandidwa+ ndi anthu koma ndi Mulungu.+ 1 Petulo 3:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Koma kukhale kwa munthu wobisika+ wamumtima, atavala zovala zosawonongeka,+ ndizo mzimu wabata ndi wofatsa+ umene uli wamtengo wapatali pamaso pa Mulungu.
60 Ndiyeno iwo anayamba kudalitsa Rabeka kuti: “Iwe mlongo wathu, ukakhale mayi wa anthu masauzande kuchulukitsa ndi masauzande 10, ndipo mbewu yako ikalande mizinda ya adani awo.”+
7 Anthu okhala m’midzi anachoka m’midzi yawo, anachoka m’midzi ya Isiraeli,+Kufikira pamene ine Debora+ ndinauka,Kufikira pamene ine ndinauka monga mayi mu Isiraeli.+
29 Koma Myuda ndi amene ali wotero mkati,+ ndipo mdulidwe wake ndi wa mumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo satamandidwa+ ndi anthu koma ndi Mulungu.+
4 Koma kukhale kwa munthu wobisika+ wamumtima, atavala zovala zosawonongeka,+ ndizo mzimu wabata ndi wofatsa+ umene uli wamtengo wapatali pamaso pa Mulungu.