Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mwaipatsa zokhumba za mtima wake,+

      Ndipo simunaimane zokhumba za pakamwa pake.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 37:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Komanso sangalala mwa Yehova,+

      Ndipo adzakupatsa zokhumba za mtima wako.+

  • Yohane 16:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kufikira nthawi ino simunapemphepo chilichonse m’dzina langa. Pemphani ndipo mudzalandira, kuti chimwemwe chanu chisefukire.+

  • 1 Yohane 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ifetu timamudalira+ kuti chilichonse chimene tingamupemphe mogwirizana ndi chifuniro chake, amatimvera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena