Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 140:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Anthu amene amakonza chiwembu mumtima mwawo,+

      Amene amandiukira tsiku lonse ngati mmene zimakhalira pankhondo.+

  • Miyambo 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 mtima wokonzera ena ziwembu,+ mapazi othamangira kukachita zoipa,+

  • Miyambo 11:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Zolakalaka za anthu olungama, ndithu n’zabwino.+ Chiyembekezo cha oipa chimabweretsa mkwiyo woopsa.+

  • Yeremiya 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsuka mtima wako ndi kuchotsa zoipa zonse, iwe Yerusalemu, kuti upulumuke.+ Kodi maganizo ako oipawo udzakhala nawo mpaka liti?+

  • Mateyu 26:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iwo anali kupangana+ zoti agwire Yesu mochenjera ndi kumupha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena