Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mudzamva kuchonderera kwa anthu ofatsa,+ inu Yehova.

      Mudzakonzekeretsa mitima yawo.+

      Mudzatchera khutu lanu,+

  • Salimo 37:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Komanso sangalala mwa Yehova,+

      Ndipo adzakupatsa zokhumba za mtima wako.+

  • Yesaya 26:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Usiku, mtima wanga umakulakalakani.+ Ndithu ndimakufunafunani ndi mtima wonse,+ chifukwa mukadzaweruza dziko lapansi,+ anthu okhala panthaka ya dzikolo adzaphunzira chilungamo.+

  • Mateyu 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Odala ndi anthu amene akumva njala ndi ludzu+ la chilungamo, chifukwa adzakhuta.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena