Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 8:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Samueli anamvera mawu onse amene anthuwo ananena, kenako anafotokozera Yehova mawuwo.+

  • Salimo 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova adzamva ndithu pempho langa loti andikomere mtima.+

      Yehova adzalandira pemphero langa.+

  • Salimo 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti waumphawi sadzaiwalidwa nthawi zonse,+

      Ndiponso chiyembekezo cha ofatsa sichidzatha konse.+

  • Salimo 102:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iye adzamvetsera pemphero la anthu amene alandidwa chilichonse,+

      Ndipo sadzapeputsa pemphero lawo.+

  • Miyambo 15:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nsembe ya anthu oipa imam’nyansa Yehova,+ koma pemphero la anthu owongoka mtima limam’sangalatsa.+

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti maso+ a Yehova* ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzero lawo,+ koma nkhope ya Yehova imakwiyira anthu ochita zoipa.”+

  • 1 Yohane 3:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 ndipo chilichonse chimene tingapemphe, iye adzatipatsa,+ chifukwa tikusunga malamulo ake ndi kuchita zinthu zomukondweretsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena