Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 31:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma ine nditapanikizika ndinati:+

      “Ndidzafafanizidwa kuchoka pamaso panu.”+

      Ndithudi mwamva kuchonderera kwanga pamene ndinali kufuulira kwa inu kupempha thandizo.+

  • Salimo 40:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Ndinayembekezera Yehova ndi mtima wonse,+

      Choncho iye anatchera khutu kwa ine ndipo anamva kufuula kwanga kopempha thandizo.+

  • Yona 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 kuti:

      “Pamene ndinali m’masautso ndinaitana Yehova,+ ndipo anandiyankha.+

      Ndinafuula kupempha thandizo ndili m’Manda* akuya.+

      Ndipo inu munamva mawu anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena