Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pakamwa pa munthu wolungama pamalankhula zinthu zanzeru,+

      Ndipo lilime lake limalankhula zinthu zachilungamo.+

  • Miyambo 22:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Tchera khutu lako ndi kumva mawu a anthu anzeru,+ kuti ulandire ndi mtima wonse nzeru zochokera kwa ine.+

  • Miyambo 22:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti n’chinthu chosangalatsa kuti uzisunge mumtima mwako,+ kuti zikhazikike pamilomo yako.+

  • Mateyu 12:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Munthu wabwino amatulutsa zabwino m’chuma chake chabwino,+ koma munthu woipa amatulutsa zoipa m’chuma chake choipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena