Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 34:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Kenako Mose mtumiki wa Yehova+ anafera pamenepo m’dziko la Mowabu, mogwirizana ndi zimene Yehova analamula.+

  • Yobu 14:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Masiku a munthu ndi odziwika,+

      Ndipo chiwerengero cha miyezi yake chili ndi inu.

      Mwamuikira lamulo kuti asalipitirire.

  • Yohane 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Inuyo nyamukani mupite ku chikondwereroko. Ine sindipitako panopa, chifukwa nthawi yanga yoyenera+ sinafike.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena