Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 26:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Ndiyeno upange chihema chopatulika ndi nsalu 10 zopangira hema.+ Nsaluzo zikhale zaulusi wopota wabwino kwambiri, ulusi wabuluu, ubweya wa nkhosa wonyika mu utoto wofiirira+ ndi ulusi wofiira kwambiri. Pansaluzo upetepo akerubi.+

  • Ekisodo 35:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Iye wawapatsa mtima wanzeru+ kuti akhale amisiri aluso pa ntchito zonse za mmisiri wolinganiza kawombedwe ka nsalu+ ndi mmisiri wopeta nsalu ndi ulusi wabuluu. Wawapatsa nzeru zimenezi kutinso achite ntchito za mmisiri wopeta nsalu ndi ubweya wa nkhosa wonyika mu utoto wofiirira, ulusi wofiira kwambiri, nsalu zabwino kwambiri, ndi ntchito za mmisiri wowomba nsalu. Watero kuti akhale amuna ogwira ntchito ina iliyonse ndi kulinganiza kapangidwe ka zinthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena